Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 31:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Aaigupto ndiwo anthu, si Mulungu; ndi akavalo ao ali nyama, si mzimu; ndipo pamene Yehova adzatambasula dzanja lace, wothandiza adzapunthwa, ndi wothandizidwa adzagwa, ndipo iwo onse awiri pamodzi adzalephera.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 31

Onani Yesaya 31:3 nkhani