Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 20:5-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Ndipo iwo adzakhala ndi mantha ndi manyazi, cifukwa ca Kusi, amene anawatama, ndi Aigupto, amene anawanyadira.

6. Ndipo wokhala m'mphepete mwa nyanja muno adzati tsiku limenelo, Taonani, kuyembekeza kwathu kuli kotero, kumene ife tinathawira atithangate kupulumutsidwa kwa mfumu ya Asuri, ndipo ife tidzapulumuka bwanji?

Werengani mutu wathunthu Yesaya 20