Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 2:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu ambiri adzanka, nati, Tiyeni tikwere kunka ku phiri la Yehova, ku nyumba ya Mulungu wa Yakobo; ndipo Iye adzatiphunzitsa za njira zace, ndipo tidzayenda m'mayendedwe ace; cifukwa m'Ziyoni mudzaturuka cilamulo, ndi mau a Yehova kucokera m'Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 2

Onani Yesaya 2:3 nkhani