Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 18:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti masika asanafike, kutatha kuphuka ndi posanduka duwa mphesa yofuna kucha, iye adzadzombolera tinthambi ndi mphopo, ndi nthambi zotasa adzazicotsa ndi kuzisadza.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 18

Onani Yesaya 18:5 nkhani