Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 18:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Yehova watero kwa ine, Ine ndidzakhala cete, ndipo ndidzayang'ana mokhala cete, ndipo ndidzayang'ana mokhalamo Ine, monga kuwala kotentha kwa dzuwa, monga mtambo wa mame m'kutentha kwa masika.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 18

Onani Yesaya 18:4 nkhani