Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 8:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo udzawayanika padzuwa, ndi pamwezi, ndi pa khamu lonse la kuthambo, limene analikonda, ndi kulitumikira, ndi kulitsata, ndi kulifuna, ndi kuligwadira; sadzasonkhanidwa, sadzaikidwa; adzakhala ndowe panthaka.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 8

Onani Yeremiya 8:2 nkhani