Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 49:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa canji udzitamandira ndi zigwa, cigwa cako coyendamo madzi, iwe mwana wamkazi wobwerera m'mbuyo, amene anakhulupirira cuma cace, nati, Adza kwa ine ndani?

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 49

Onani Yeremiya 49:4 nkhani