Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 45:2-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Yehova Mulungu wa Israyeli atero kwa inu, Baruki:

3. Munati, Kalanga ine tsopano! pakuti Yehova waonjezera cisoni pa zowawa zanga; ndalema ndi kubuula kwanga, sindipeza kupuma,

4. Uzitero naye, Yehova atero: Taonani, cimene ndamanga ndidzapasula, ndi cimene ndaoka ndidzazula; ndidzatero m'dziko lonseli.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 45