Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 44:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israyeli: Taonani, ndidzayang'anitsa nkhope yanga pa inu ndikucitireni inu coipa, ndidule Yuda lonse.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 44

Onani Yeremiya 44:11 nkhani