Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 44:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzatengaotsala a Yuda, amene analozetsa nkhope zao alowe m'dziko la Aigupto akhale m'menemo, ndipo adzathedwa onse; m'dziko la Aigupto adzagwa, adzathedwa ndi lupanga ndi njala; adzafa kuyambira wamng'ono mpaka wamkuru, ndi lupanga ndi njala; ndipo adzakhala citukwano, ndi cizizwitso, ndi citemberero, ndi citonzo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 44

Onani Yeremiya 44:12 nkhani