Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 41:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali, pamene analowa pakati pa mudzi, Ismayeli mwana, wa Netaniya anawapha, nawaponya pakati pa dzenje, iye ndi anthu okhala naye.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 41

Onani Yeremiya 41:7 nkhani