Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 34:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Zedekiya mfumu ya Yuda ndi akulu ace ndidzawapereka m'dzanja la adani ao, ndi m'dzanja la akufuna moyo wao, ndi m'dzanja la nkhondo ya mfumu ya ku Babulo, imene yakucokerani.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 34

Onani Yeremiya 34:21 nkhani