Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 29:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

cifukwa sanamvera mau anga, ati Yehova, amene ndinawatumizira ndi atumiki anga aneneri, ndi kuuka mamawa ndi kuwatuma, koma munakana kumva, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 29

Onani Yeremiya 29:19 nkhani