Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 25:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndi mafumu onse a kumpoto, a kutari ndi a kufupi, wina ndi mnzace; ndi maufumu onse a dziko lapansi, okhala pansi pano; ndi mfumu ya Sesaki adzamwa pambuyo pao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25

Onani Yeremiya 25:26 nkhani