Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 23:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Taonani, Ine ndidana ndi amene anenera maloto onama, ndi kuwafotokoza ndi kusokeretsa anthu anga ndi zonama zao, ndi matukutuku ao acabe; koma Ine sindinatuma iwo, sindinauza iwo; sadzapindulira konse anthu awa, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 23

Onani Yeremiya 23:32 nkhani