Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 22:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

amene ati, Ndidzadzimangira ndekha nyumba yotakata ndi zipinda zapamwamba zazikuru, nadziboolera mazenera; nabvundima chindwi lam'kati ndi mikungudza, naipaka ndi utoto wofiira.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 22

Onani Yeremiya 22:14 nkhani