Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 20:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Pasuri anampanda Yeremiya mneneriyo, namuika matangadza amene anali m'cipata ca kumtunda ca Benjamini, cimene cinali ku nyumba ya Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 20

Onani Yeremiya 20:2 nkhani