Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 16:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akuru ndi ang'onong'ono adzafa m'dziko muno; sadzaikidwa, anthu sadzacita maliro ao, sadzadziceka, sadzadziyeseza adazi, cifukwa ca iwo;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 16

Onani Yeremiya 16:6 nkhani