Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 13:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace uzinena ndi iwo mau awa: Atero Yehova, Mulungu wa Israyeli, Matumba onse adzadzazidwa ndi vinyo; ndipo adzati kwa iwe, Kodi sitidziwitsa bwino kuti matumba onse adzadzazidwa ndi vinyo?

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 13

Onani Yeremiya 13:12 nkhani