Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 13:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anthu oipa awa, amene akana kumva mau anga, amene ayenda m'kuumirira kwa mtima wao, atsata milungu yina kuitumikira, ndi kuigwadira, adzakhala ngati mpango uwu, wosayenera kanthu.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 13

Onani Yeremiya 13:10 nkhani