Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nyimbo 5:14-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Manja ace akunga zing'anda zagolidi zoikamo zonyezimira zoti biriwiri:Thupi lace likunga copanga ca minyanga colemberapo masafiro.

15. Miyendo yace ikunga zoimiritsa za mwala wonyezimira,Zogwirika m'kamwa mwa golidi:Maonekedwe ace akunga Lebano, okometsetsa ngati mikungudza.

16. M'kamwa mwace muli mokoma: inde, ndiye wokondweretsa ndithu.Ameneyu ndi wokondedwa wanga, ameneyu ndi bwenzi langa,Ana akazi inu a ku Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu Nyimbo 5