Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 8:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mose ndi Aroni ndi khamu lonse la ana a Israyeli anacitira Alevi monga mwa zonse Yehova adauza Mose kunena za Alevi; momwemo ana a lsrayeli anawacitira.

Werengani mutu wathunthu Numeri 8

Onani Numeri 8:20 nkhani