Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 8:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndapereka Alevi akhale mphatso ya kwa Aroni ndi ana ace amuna yocokera mwa ana a Israyeli, kucita nchito ya ana a Israyeli, m'cihema cokomanako ndi kucita cotetezera ana a Israyeli; kuti pasakhale mliri pakati pa ana a Israyeli, pakuyandikiza ana a Israyeli ku malo opatulika.

Werengani mutu wathunthu Numeri 8

Onani Numeri 8:19 nkhani