Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 22:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Balaki anati kwa Balamu, Kodi sindinatumiza kwa iwe ndithu kukakuitana? Unalekeranji kudza kwa ine? sindikhoza kodi kukucitira ulemu?

Werengani mutu wathunthu Numeri 22

Onani Numeri 22:37 nkhani