Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 21:34-35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Ndipo Yehova anati kwa Mose, Usamuopa; popeza ndampereka m'manja mwako, iye ndi anthu ace onse, ndi dziko lace; umcitire monga umo unacitira Sihoni mfumu ya Aamori anakhalayo ku Hesiboni.

35. Ndipo anamkantha iye, ndi ana ace amuna ndi anthu ace onse, kufikira sanatsala ndi mmodzi yense; nalanda dziko lace likhale lao lao.

Werengani mutu wathunthu Numeri 21