Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 16:38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

mbale zofukizazo za iwo amene adacimwira moyo wao wao, ndipo azisule zaphanthiphanthi, zikhale cibvundikilo ca guwa la nsembe; popeza anabwera nazo pamaso pa Yehova, cifukwa cace zikhala zopatulika; ndipo zidzakhala cizindikilo kwa ana a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Numeri 16

Onani Numeri 16:38 nkhani