Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 11:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo ndidzatsika ndi kulankhula nawe komweko; ndipo ndidzatengako mzimu uti pa iwe, ndi kuika pa iwowa; adzakuthandiza kusenza katundu wa anthu awa, kuti usasenze wekha.

Werengani mutu wathunthu Numeri 11

Onani Numeri 11:17 nkhani