Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Numeri 11:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa Mose, Undisonkhanitsire amuna makumi asanu ndi awiri mwa akuru a Israyeli, amene uwadziwa kuti ndiwo akuru a anthu, ndi akapitao ao; nubwere nao ku cihema cokomanako, kuti aimeko pamodzi ndi iwe.

Werengani mutu wathunthu Numeri 11

Onani Numeri 11:16 nkhani