Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 9:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anaimirira pa ciunda ca Alevi Yesuwa, ndi Bani, Kadimiyeli, Sebaniya, Buni, Serebiya, Bani, ndi Kenani, napfuula ndi mau akuru kwa Yehova Mulungu wao.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 9

Onani Nehemiya 9:4 nkhani