Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 8:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Nehemiya, ndiye kazembe, ndi Ezara wansembe mlembiyo, ndi Alevi ophunzitsa anthu, ananena ndi anthu onse, Lero ndilo lopatulikira Yehova Mulungu wanu, musamacita maliro, musamalira misozi. Popeza anthu onse analira misozi pakumva mau a cilamulo.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 8

Onani Nehemiya 8:9 nkhani