Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 7:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ana a dziko amene anakwera kucokera kundende a iwo adatengedwa ndende, amene Nebukadinezara mfumu ya Babulo adawatenga, anabwera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, yense ku mudzi wace, ndi awa:

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7

Onani Nehemiya 7:6 nkhani