Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 7:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mulungu wanga anaika m'mtima mwanga kuti ndiwasonkhanitse aufuru, ndi olamulira, ndi anthu, kuti awerengedwe mwa cibadwidwe cao. Ndipo ndinapeza buku la cibadwidwe la iwo adakwerako poyamba paja; ndinapeza mudalembedwa m'mwemo.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 7

Onani Nehemiya 7:5 nkhani