Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Nehemiya 3:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi cipata ca kukasupe anacikonza Saluni mwana wa Koli, Hoze mkuru wa dziko la Mizipa anacimanga, nacikomaniza pamwamba pace, naika zitseko zace, zokowera zace, ndi mipiringidzo yace; ndiponso linga la dziwe la Sela pa munda wa mfumu, ndi kufikira ku makwerero otsikira ku mudzi wa Davide.

Werengani mutu wathunthu Nehemiya 3

Onani Nehemiya 3:15 nkhani