5. Pamenepo anaopa kwakukuru, popanda cifukwa ca kuopa:Pakuti Mulungu anamwaza mafupa a iwo akuzinga iwe;Unawacititsa manyazi, pakuti Mulungu anawakaniza.
6. Ha, cipulumutso ca Israyeli cicokere m'Ziyoni!Pakubweretsa Mulungu anthu ace a m'ndende,Yakobo adzakondwera, Israyeli adzasekera.