Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 53:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anaopa kwakukuru, popanda cifukwa ca kuopa:Pakuti Mulungu anamwaza mafupa a iwo akuzinga iwe;Unawacititsa manyazi, pakuti Mulungu anawakaniza.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 53

Onani Masalmo 53:5 nkhani