Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 40:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Inu, Yehova, Mulungu wanga, zodabwiza zanu mudazicita nzambiri,Ndipo zolingirira zanu za pa ife;Palibe wina wozifotokozera Inu;Ndikazisimba ndi kuzichula, Zindicurukira kuziwerenga.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 40

Onani Masalmo 40:5 nkhani