Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 40:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Kuyembekeza ndayembekeza Yehova;Ndipo anandilola, namva kupfuula kwanga.

2. Ndipo anandikweza kunditurutsa m'dzenje la citayiko, ndi m'thope la pacithaphwi;Nandipondetsa pathanthwe, nakhazika mayendedwe anga.

3. Ndipo anapatsa Nyimbo yatsopano m'kamwa mwanga, cilemekezo ca kwa Mulungu wanga;Ambiri adzaciona, nadzaopa,Ndipo adzakhulupirira Yehova.

4. Wodala munthuyo wakuyesa Yehova wokhulupirika;Wosasamala odzikuza, ndi opatukira kubodza.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 40