Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 17:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo uzinena nao, Munthu ali yense wa mbumba ya Israyeli, kapena mlendo wakugonera pakati panu, amene apereka nsembe yopsereza kapena nsembe yophera,

Werengani mutu wathunthu Levitiko 17

Onani Levitiko 17:8 nkhani