Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 17:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ali yense wakudya yakufa yokha, kapena yojiwa kuthengo, ngakhale ndiye wa m'dziko kapena mlendo, azitsuka nsaru zace, nasambe ndi madzi, nadzakhala wodetsedwa kufikira madzulo; pamenepo adzakhala woyera.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 17

Onani Levitiko 17:15 nkhani