Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 17:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti moyo wa nyama ukhala m'mwazi; ndipo ndakupatsani uwu pa guwa la nsembe, ucite cotetezera moyo wanu; pakuti wocita cotetezera ndiwo mwazi, cifukwa ca moyo wace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 17

Onani Levitiko 17:11 nkhani