Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 17:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo munthu ali yense wa mbumba ya Israyeli, kapena mlendo wogonera pakati panu, wakudya mwazi uli wonse; nkhope yanga idzatsutsana naye munthu wakudya mwaziyo, ndi kumsadza kumcotsa kwa anthu a mtundu wace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 17

Onani Levitiko 17:10 nkhani