Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 7:14-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Ndipo sanapfuulira kwa Ine ndi mtima wao, koma alira pakama pao, asonkhanira tirigu ndi vinyo, apikisana ndi Ine.

15. Cinkana ndawalangiza ndi kulimbitsa manja ao, andilingiririra coipa,

16. Abwerera, koma si kwa Wam'mwambayo; akunga uta wosakhulupirika; akalonga ao adzagwa ndi lupanga mwa cipongwe ca lilime lao; ici ndico adzawasekera m'dziko la Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 7