Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 7:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tsoka kwa iwowa! pakuti anandizembera; cionongeko kwa iwowa! pakuti anandilakwira; ndikadawalanditsa Ine, koma anandinenera zabodza.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 7

Onani Hoseya 7:13 nkhani