Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 5:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndidzakhala kwa Efraimu ngati mkango, ndi kwa nyumba ya Yuda ngati msona wa mkango; ndidzamwetula Ine ndi kucoka; ndidzanyamula, ndipo palibe wakulanditsa.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 5

Onani Hoseya 5:14 nkhani