Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 47:30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma pamene ndidzagona ndi makolo anga, udzanditenge ine kuturuka m'dziko la Aigupto, ukandiike ine m'manda mwao. Ndipo iye anati, Ndidzacita monga mwanena.

Werengani mutu wathunthu Genesis 47

Onani Genesis 47:30 nkhani