Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 43:8-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Ndipo Yuda anati kwa atate wace Israyeli, Mumtume mnyamata pamodzi ndi ine ndipo ife tidzanyamuka ndi kupita; kuti tikhale ndi moyo tisafe, ife ndi inu ndi ana athu ang'ono.

9. Ine ndidzakhala cikole, pa manja anga mudzamfunsa: ndikapanda kumbwezera kwa inu ndi kumuimitsa pamaso panu, cifukwa cace cidzakhala pa ine masiku onse:

10. pakuti tikadaleka kucedwa mwenzi tsopano titabwera kawiri.

Werengani mutu wathunthu Genesis 43