Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 11:30-32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

30. Koma Sarai anali wouma; analibe mwana.

31. Ndipo Tera anatenga Abramu mwana wace wamwamuna, ndi Loti mwana wa Harana, mwana wace wamwamuna, ndi Sarai mpongozi wace, mkazi wa mwana wace Abramu; ndipo anaturuka pamodzi nao ku Uri wa kwa Akaldayo kuti amuke ku dziko la Kanani, ndipo anafika ku Harana, nakhala kumeneko.

32. Masiku a Tera anali zaka mazana awiri kudza zisanu; ndipo anafa Tera m'Harana.

Werengani mutu wathunthu Genesis 11