Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 11:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Tera anatenga Abramu mwana wace wamwamuna, ndi Loti mwana wa Harana, mwana wace wamwamuna, ndi Sarai mpongozi wace, mkazi wa mwana wace Abramu; ndipo anaturuka pamodzi nao ku Uri wa kwa Akaldayo kuti amuke ku dziko la Kanani, ndipo anafika ku Harana, nakhala kumeneko.

Werengani mutu wathunthu Genesis 11

Onani Genesis 11:31 nkhani