Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 6:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ndidzasiyapo otsala, popeza mudzakhala nao ena akupulumuka lupanga mwa amitundu pobalalitsidwa inu m'maiko maiko.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 6

Onani Ezekieli 6:8 nkhani