Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 44:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akhale nao akapa abafuta pamitu pao, ndi akabudula m'cuuno mwao; asabvale m'cuuno kanthu kali konse kakucititsa thukuta.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 44

Onani Ezekieli 44:18 nkhani